Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Yehova Mulungu wanu adzabweza kwawo anthu a mtundu wanu amene anagwidwa nʼkupita kudziko lina,+ ndipo adzakuchitirani chifundo+ nʼkukusonkhanitsaninso pamodzi kuchokera pakati pa anthu onse kumene Yehova Mulungu wanu anakubalalitsirani.+

  • Salimo 30:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Salimo 85:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 85 Inu Yehova, dziko lanu mwalisonyeza kukoma mtima.+

      Mwabwezeretsa ana a Yakobo amene anagwidwa ukapolo.+

  • Salimo 126:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 40:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Mulankhuleni Yerusalemu momufika pamtima.*

      Muuzeni kuti ntchito imene ankagwira mokakamizidwa yatha,

      Komanso kuti malipiro a zolakwa zake aperekedwa.+

      Kuchokera mʼdzanja la Yehova, iye walandira malipiro okwanira* a machimo ake onse.”+

  • Yesaya 66:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani