Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 56:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndipo alendo amene abwera kwa Yehova kuti amutumikire,

      Kuti azikonda dzina la Yehova+

      Ndiponso kuti akhale atumiki ake,

      Onse amene amasunga Sabata ndipo salidetsa

      Komanso amene amatsatira pangano langa,

       7 Nawonso ndidzawabweretsa kuphiri langa loyera+

      Ndipo ndidzawachititsa kuti asangalale mʼnyumba yanga yopemphereramo.

      Nsembe zawo zopsereza zathunthu ndi nsembe zawo zina ndidzazilandira paguwa langa lansembe.

      Chifukwa nyumba yanga idzatchedwa nyumba yopemphereramo anthu a mitundu yonse.”+

  • Yesaya 60:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mitundu ya anthu idzatsata kuwala kwako,+

      Ndipo mafumu+ adzatsata ulemerero wako wonyezimira.*+

  • Zekariya 8:22, 23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani