Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Nehemiya 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 44:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 62:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 62 Chifukwa cha Ziyoni sindidzakhala chete,+

      Ndipo chifukwa cha Yerusalemu sindidzakhala phee

      Mpaka kulungama kwake kutawala kwambiri,+

      Ndiponso mpaka chipulumutso chake chitakhala ngati muuni woyaka moto.+

  • Yeremiya 31:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Chifukwa tsiku lidzafika limene alonda amene ali mʼmapiri a Efuraimu adzafuula kuti:

      ‘Nyamukani, tiyeni tipite ku Ziyoni kwa Yehova Mulungu wathu.’”+

  • Zekariya 1:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Fuulanso kuti, ‘Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti: “Mizinda yanga idzasefukiranso ndi zinthu zabwino. Yehova adzalimbikitsanso Ziyoni+ ndipo adzasankhanso Yerusalemu.”’”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani