Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Hoseya 14:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Efuraimu adzanena kuti, ‘Mafano alibenso ntchito kwa ine.’+

      Ine ndidzamva ndipo ndidzamuyangʼanira.+

      Ndidzakhala ngati mtengo wa mkungudza wobiriwira bwino.

      Ndipo mudzapeza zipatso kwa ine.”

  • Zekariya 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti, “Pa tsiku limenelo, ndidzafufuta mayina a mafano mʼdziko lonseli+ ndipo sadzakumbukiridwanso. Ndidzachotsamo aneneri+ komanso mzimu wonyansa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani