Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 8:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Mumve pemphero lopempha chifundo la mtumiki wanu komanso la anthu anu Aisiraeli, limene angapemphere atayangʼana malo ano. Inuyo mumve muli kumalo anu okhala, kumwamba,+ mumve nʼkukhululuka.+

  • 2 Mbiri 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mbiri 20:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 ‘Tsoka likatigwera, kaya lupanga, chiweruzo chowawa, mliri kapena njala, tiziima patsogolo pa nyumbayi ndi pamaso panu (popeza dzina lanu lili mʼnyumbayi)+ nʼkufuulira inu kuti mutithandize pa mavuto athu, ndipo inu muzitimva nʼkutipulumutsa.’+

  • Danieli 9:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho ndinayangʼana kwa Yehova Mulungu woona ndipo ndinapemphera momuchonderera, ndinasala kudya,+ ndinavala ziguduli komanso kudzithira phulusa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani