Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 19:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno Yesaya mwana wa Amozi anatumiza uthenga kwa Hezekiya, wakuti: “Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena kuti, ‘Ndamva pemphero lako+ lokhudza Senakeribu mfumu ya Asuri.+ 21 Awa ndi mawu otsutsana naye amene Yehova wanena:

      “Namwali, mwana wamkazi wa Ziyoni, wakunyoza ndipo wakunyodola.

      Mwana wamkazi wa Yerusalemu wakupukusira mutu.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani