10 Dzanja langa lagwira maufumu olambira milungu yopanda phindu,
Amene zifaniziro zawo zogoba zinali zambiri kuposa za ku Yerusalemu ndi ku Samariya.+
11 Kodi zimene ndachitira Samariya ndi milungu yake yopanda phindu,+
Si zimenenso ndidzachitire Yerusalemu ndi mafano ake?’