Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 19:29-31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Ichi chidzakhala chizindikiro chanu:* Chaka chino mudya mbewu zimene zamera zokha. Mʼchaka chachiwiri mudzadya mbewu zophuka kuchokera ku mbewu zimenezi.+ Koma mʼchaka chachitatu, mudzadzala mbewu nʼkukolola ndipo mudzalima minda ya mpesa nʼkudya zipatso zake.+ 30 Anthu amʼnyumba ya Yuda amene adzapulumuke, amene adzatsale,+ adzakhala ngati mitengo imene yazika mizu pansi nʼkubereka zipatso zambiri. 31 Chifukwa anthu otsala adzachokera ku Yerusalemu ndipo opulumuka adzachokera kuphiri la Ziyoni. Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzachita zimenezi modzipereka kwambiri.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani