Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba akanapanda kutisiyira anthu ochepa opulumuka,

      Tikanakhala ngati Sodomu,

      Ndipo tikanafanana ndi Gomora.+

  • Yesaya 10:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsiku limenelo, otsala a Isiraeli

      Ndi amʼnyumba ya Yakobo amene adzapulumuke

      Sadzadaliranso amene anawamenya,+

      Koma ndi mtima wonse adzadalira Yehova,

      Woyera wa Isiraeli.

      21 Otsala okha ndi amene adzabwerere,

      Otsala a Yakobo adzabwerera kwa Mulungu Wamphamvu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani