Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 19:32-34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Choncho Yehova wanena izi zokhudza mfumu ya Asuri:+

      “Sadzalowa mumzindawu+

      Kapena kuponyamo muvi

      Kapena kufikamo ndi chishango

      Kapenanso kumanga malo okwera omenyerapo nkhondo atauzungulira.+

      33 Adzabwerera kudzera njira imene anadutsa pobwera,

      Ndipo sadzalowa mumzindawu.” Watero Yehova.

      34 “Ndidzateteza mzindawu+ ndipo ndidzaupulumutsa chifukwa cha ineyo+

      Ndiponso chifukwa cha mtumiki wanga Davide.”’”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani