Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Genesis 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 54:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mapiri akhoza kuchotsedwa,

      Ndipo zitunda zikhoza kugwedezeka,

      Koma chikondi changa chokhulupirika sichidzachotsedwa pa iwe,+

      Ndipo pangano langa lamtendere silidzagwedezeka,”+ akutero Yehova, amene akukuchitira chifundo.+

  • Yeremiya 31:35-37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yehova amene amapereka dzuwa kuti liziwala masana,

      Amene amaika malamulo oti mwezi ndi nyenyezi ziziwala usiku,

      Amene amavundula nyanja

      Kuti mafunde ake achite phokoso,

      Amene dzina lake ndi Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, wanena kuti:+

      36 “‘Ngati malamulo amenewa angalephere kugwira ntchito yake,

      Ndiye kutinso mbadwa za Isiraeli zingasiye kukhala mtundu, umene umakhala pamaso panga nthawi zonse,’ akutero Yehova.”+

      37 Yehova wanena kuti: “‘Ngati kumwamba kungayezedwe ndipo ngati maziko a dziko lapansi angafufuzidwe, ndiye kuti inenso ndingakane mbadwa zonse za Isiraeli chifukwa cha zonse zimene achita,’ akutero Yehova.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani