Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 25:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Gedaliya analumbirira akuluakuluwo ndi asilikali awo kuti: “Musaope kukhala atumiki a Akasidi. Khalani mʼdzikoli nʼkumatumikira mfumu ya Babulo ndipo zinthu zikuyenderani bwino.”+

  • Yeremiya 27:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma mtundu wa anthu umene udzaike khosi lake mʼgoli la mfumu ya Babulo nʼkuitumikira, ndidzaulola kuti ukhalebe* mʼdziko lawo ndipo udzalima minda nʼkumakhala mʼdzikolo,’ akutero Yehova.”’”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani