Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mafumu 25:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Zitatero, anthu onse, kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu komanso akuluakulu a magulu a asilikali, anathawira ku Iguputo,+ chifukwa ankaopa Akasidi.+

  • Yeremiya 42:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 ponena kuti, “Ayi, mʼmalomwake tipita kudziko la Iguputo,+ kumene sitidzaona nkhondo kapena kumva kulira kwa lipenga komanso kumene sitidzasowa chakudya. Ife tizikakhala kumeneko,”

  • Yeremiya 43:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iwo anapita mʼdziko la Iguputo chifukwa sanamvere mawu a Yehova ndipo anakafika ku Tahapanesi.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani