-
Yeremiya 25:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+
-
-
Yeremiya 25:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Kenako ndinamwetsanso Farao mfumu ya Iguputo, atumiki ake, akalonga ake ndi anthu ake onse+
-
-
Ezekieli 30:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 Lupanga lidzabwera kudzaukira Iguputo, ndipo anthu a ku Itiyopiya adzachita mantha kwambiri anthu akadzaphedwa ku Iguputo.
Chuma cha Iguputo chidzalandidwa ndipo maziko ake adzagwetsedwa.+
-