Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 42:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndipo amuna onse amene atsimikiza mtima kupita ku Iguputo kuti akakhale kumeneko adzafa ndi lupanga, njala ndi mliri.* Palibe amene adzapulumuke kapena kuthawa tsoka limene ndidzawagwetsere.”’

      18 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti: ‘Mofanana ndi mmene ndinasonyezera anthu okhala mu Yerusalemu+ mkwiyo ndi ukali wanga, inunso ndidzakusonyezani mkwiyo wanga ngati mutapita ku Iguputo. Mudzakhala otembereredwa, chinthu chochititsa mantha, chinthu chonyozeka+ ndi chochititsa manyazi ndipo malo ano simudzawaonanso.’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani