Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 66:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova adzapereka chiweruzo pogwiritsa ntchito moto,

      Inde adzagwiritsa ntchito lupanga lake poweruza anthu onse,

      Ndipo anthu ophedwa ndi Yehova adzakhala ambiri.

  • Yeremiya 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+

  • Yeremiya 25:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 mafumu onse akumpoto, akutali ndi apafupi, mmodzi ndi mmodzi ndipo ndinamwetsanso maufumu ena onse apadziko lapansi. Koma mfumu ya Sesaki*+ idzamwa pambuyo pa onsewa.

  • Zefaniya 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova wanena kuti: ‘Choncho pitirizani kundiyembekezera,*+

      Mpaka tsiku limene ndidzanyamuke kuti ndikatenge zinthu za anthu omwe ndawagonjetsa.*

      Chiweruzo changa ndi choti ndisonkhanitse mitundu ya anthu, ndisonkhanitse maufumu,

      Kuti ndiwasonyeze mkwiyo wanga, ndithu mkwiyo wanga wonse woyaka moto,+

      Chifukwa moto wa mkwiyo wanga udzawotcheratu dziko lonse lapansi.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani