Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 11:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Zefaniya 1:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 “Ndidzatambasula dzanja langa nʼkuwononga Yuda,

      Ndiponso anthu onse okhala mu Yerusalemu.

      Ndidzawononga chilichonse chokhudza Baala+ pamalowa.

      Ndidzawononganso ansembe komanso dzina la ansembe a mulungu wachilendo.+

       5 Ndidzawononga anthu amene amakwera padenga nʼkumagwadira magulu a zinthu zakumwamba.*+

      Komanso amene amagwada ndiponso kulumbira kuti adzakhala okhulupirika kwa Yehova+

      Koma nʼkumalumbiranso kuti adzakhala okhulupirika kwa Malikamu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani