Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 51:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 “Kwezani chizindikiro mʼdzikoli.+

      Imbani lipenga pakati pa mitundu ya anthu.

      Sankhani* mitundu ya anthu kuti ichite naye nkhondo.

      Muitanireni maufumu a ku Ararati,+ ku Mini ndi ku Asikenazi+ kuti adzamuukire.

      Muikireni wolemba anthu usilikali.

      Mubweretsereni mahatchi ambiri ngati dzombe lingʼonolingʼono.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani