Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 137:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iwe mwana wamkazi wa Babulo,* amene watsala pangʼono kuwonongedwa,+

      Wosangalala adzakhala amene adzakubwezere

      Zimene iwe watichitira.+

  • Yeremiya 50:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Itanani anthu oponya mivi ndi uta kuti adzaukire Babulo,

      Anthu onse amene akukunga uta.+

      Mangani misasa momuzungulira. Pasapezeke wothawa.

      Mubwezereni zimene anachita.+

      Muchitireni zonse zimene iye anachita.+

      Chifukwa iye wachita zinthu modzikuza pamaso pa Yehova,

      Pamaso pa Woyera wa Isiraeli.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani