Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ezekieli 21:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa mfumu ya Babulo idzaima pamalo pamene misewu iwiriyo yagawikana kuti iwombeze maula. Mfumuyo idzagwedeza mivi, idzafunsira kwa mafano ake* komanso idzawombeza maula pogwiritsa ntchito chiwindi cha nyama. 22 Maula amene adzakhale mʼdzanja lake lamanja, adzasonyeza kuti apite ku Yerusalemu, akaike zida zogumulira mzindawo, akalamule asilikali ake kuti aphe anthu, akalize chizindikiro cha nkhondo, akaike zida zogumulira mageti a mzindawo, akamange malo okwera omenyerapo nkhondo ndiponso kuti akamange mpanda womenyerapo nkhondo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani