Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Yehova wanena kuti: “Tsoka kwa ana aamuna osamvera,+

      Amene amachita zofuna zawo osati zofuna zanga,+

      Amene amapanga mgwirizano* koma osati motsogoleredwa ndi mzimu wanga,

      Kuti awonjezere tchimo pa tchimo.

  • Yesaya 48:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Chifukwa ndinadziwa kuti ndinu anthu ouma khosi,

      Kuti khosi lanu lili ngati mtsempha wachitsulo ndiponso kuti chipumi chanu chili ngati kopa,*+

  • Yeremiya 5:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma anthu awa ali ndi mtima wosamvera komanso wopanduka.

      Achoka panjira yanga ndipo akuyenda mʼnjira yawo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani