Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 4:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Yehova wanena kuti: “Dziko lonseli lidzakhala bwinja,+

      Koma sindidzaliwonongeratu.

  • Yeremiya 25:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Dziko lonseli lidzakhala bwinja ndipo lidzakhala chinthu chochititsa mantha. Mitundu imeneyi idzatumikira mfumu ya ku Babulo zaka 70.”’+

  • Yeremiya 32:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Anthu adzagulanso minda mʼdziko lino,+ ngakhale mukunena kuti: “Dziko ili ndi bwinja, lopanda munthu wokhalamo kapena nyama yakutchire ndipo laperekedwa kwa Akasidi.”’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani