Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Nʼchifukwa chiyani tikungokhala pano?

      Tiyeni tisonkhane pamodzi ndipo tilowe mʼmizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri+ kuti tikafere kumeneko.

      Chifukwa Yehova Mulungu wathu adzatiwononga,

      Ndipo amatipatsa madzi apoizoni kuti timwe,+

      Chifukwa tachimwira Yehova.

  • Yeremiya 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wadzudzula aneneriwo kuti:

      “Ndiwadyetsa chitsamba chowawa

      Ndipo ndiwapatsa madzi apoizoni kuti amwe.+

      Chifukwa kuchokera mwa aneneri a ku Yerusalemu mpatuko wafalikira mʼdziko lonse.”

  • Maliro 3:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Wandikhutitsa zinthu zowawa ndipo wandichititsa kuti ndidye chitsamba chowawa.+

  • Maliro 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kumbukirani kuti ndikuvutika ndipo ndilibe pokhala.+ Kumbukiraninso kuti ndimadya chitsamba chowawa ndi poizoni wowawa.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani