Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 4:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ine ndamva mawu angati a mkazi amene akumva ululu,

      Ndamva ngati kubuula kwa mkazi amene akubereka mwana wake woyamba,

      Koma ndi mawu a mwana wamkazi wa Ziyoni* amene akupuma movutikira.

      Iye akutambasula manja ake nʼkunena kuti:+

      “Mayo ine, ndatopa ndi anthu amene akufuna kundipha!”

  • Ezekieli 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anthu awo amene adzapulumuke adzathawira kumapiri ndipo mofanana ndi njiwa zamʼzigwa, aliyense adzalira chifukwa cha zolakwa zake.+

  • Mika 1:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Chifukwa cha zimenezi ndidzalira ndi kufuula.+

      Ndidzayenda wopanda nsapato komanso wosavala.+

      Ndidzalira ngati mimbulu,

      Ndiponso ngati nthiwatiwa.

       9 Bala lake ndi losachiritsika,+

      Ndipo lakafika mpaka ku Yuda.+

      Mliri umenewu wafalikira mpaka kukafika pageti la anthu amtundu wanga ku Yerusalemu.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani