Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 36:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho anawabweretsera mfumu ya Akasidi+ yomwe inapha anyamata awo ndi lupanga+ mʼnyumba yopatulika.+ Sinamvere chisoni mnyamata kapena namwali, wachikulire kapena wodwala.+ Mulungu anapereka zonse mʼmanja mwake.+

  • Yeremiya 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova,

      Ndipo ndatopa ndi kuusunga.”+

      “Tsanulirani mkwiyowo pa mwana amene ali mumsewu,+

      Pa gulu la anyamata amene asonkhana pamodzi.

      Onse adzagwidwa, mwamuna limodzi ndi mkazi wake,

      Anthu achikulire limodzi ndi anthu okalamba.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani