Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Nʼchifukwa chake mkwiyo wa Yehova wayakira anthu ake,

      Ndipo adzatambasula dzanja lake nʼkuwalanga.+

      Mapiri adzagwedezeka,

      Ndipo mitembo yawo idzakhala ngati zinyalala mʼmisewu.+

      Chifukwa cha zonsezi, mkwiyo wake sunabwerere,

      Koma dzanja lake lidakali lotambasula kuti awalange.

  • Yeremiya 16:3, 4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ponena za ana aamuna ndi ana aakazi amene adzabadwe mʼmalo ano, komanso ponena za amayi ndi abambo amene adzabereke anawo mʼdzikoli, Yehova akuti: 4 ‘Iwo adzafa ndi matenda oopsa+ koma palibe amene adzalire maliro awo kapena kuwaika mʼmanda. Iwo adzakhala ngati manyowa panthaka.+ Adzafa ndi lupanga ndiponso njala.+ Mitembo yawo idzakhala chakudya cha mbalame zamumlengalenga ndi zilombo zakutchire.’

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani