Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+

  • Yeremiya 25:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Ndinamwetsanso Dedani,+ Tema, Buza, onse odulira ndevu zawo zamʼmbali,+

  • Yeremiya 49:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ngamila zawo zidzalandidwa,

      Ndipo ziweto zawo zochulukazo zidzatengedwa ndi adani.

      Anthu amene amadulira ndevu zawo zamʼmbali,

      Ndidzawabalalitsira kumbali zonse,*+

      Ndipo ndizawagwetsera tsoka kuchokera kumadera onse,” akutero Yehova.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani