-
Ezekieli 6:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Iwo adzadziwa kuti ine ndine Yehova,+ mitembo ya anthu awo ikadzakhala pakati pa mafano awo onyansa, kuzungulira maguwa awo onse ansembe,+ paphiri lililonse lalitali, pansonga zonse za mapiri, pansi pa mtengo uliwonse waukulu wamasamba obiriwira, ndiponso pansi pa nthambi za mitengo ikuluikulu pamene ankaperekerapo nsembe zonunkhira kuti asangalatse mafano awo onse onyansa.+
-