-
2 Mafumu 24:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 Nebukadinezara mfumu ya Babulo, anabwera kudzamenyana ndi anthu amumzindawo atumiki ake atauzungulira.
-
-
Yeremiya 15:13Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
13 Chuma chanu komanso zinthu zanu zamtengo wapatali ndidzazipereka kwa adani anu kuti azitenge.+
Adzazitenga popanda malipiro chifukwa cha machimo anu onse amene munachita mʼdziko lanu lonse.
-