Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Nʼchifukwa chake mkwiyo wa Yehova wayakira anthu ake,

      Ndipo adzatambasula dzanja lake nʼkuwalanga.+

      Mapiri adzagwedezeka,

      Ndipo mitembo yawo idzakhala ngati zinyalala mʼmisewu.+

      Chifukwa cha zonsezi, mkwiyo wake sunabwerere,

      Koma dzanja lake lidakali lotambasula kuti awalange.

  • Yeremiya 15:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzazipereka kwa adani anu

      Kuti azitenge nʼkupita nazo kudziko limene simukulidziwa.+

      Chifukwa mkwiyo wanga wayatsa moto,

      Ndipo motowo ukukuyakirani.”+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani