- 
	                        
            
            Yeremiya 23:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
- 
                            - 
                                        26 Kodi maganizo onena zabodza apitiriza kukhala mumtima mwa aneneriwa mpaka liti? Iwo ndi aneneri amene amanena chinyengo chochokera mumtima mwawo.+ 
 
-