Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 7:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mafumu 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Chipilala chilichonse chinali chachitali mikono 18*+ ndipo mutu wake unali wakopa. Mutuwo unali wautali mikono itatu ndipo maukonde ndi makangaza* amene anazungulira mutuwo, onse anali akopa.+ Chipilala chachiwiri ndi maukonde ake chinalinso chofanana ndi choyambacho.

  • 2 Mbiri 4:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yeremiya 52:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ponena za zipilalazo, chipilala chilichonse chinali chachitali mamita 8* ndipo chinkatha kuzunguliridwa ndi chingwe chachitali mamita 5.*+ Chipilala chilichonse chinali ndi mphako mkati ndipo kuchindikala kwake kunali masentimita 7.*

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani