-
Ezekieli 16:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Unatenga zovala zako zina za mitundu yosiyanasiyana nʼkukongoletsera malo okwezeka pamene unkachitirapo uhule.+ Zinthu zimene siziyenera kuchitika ndipo zisadzachitikenso.
-
-
Ezekieli 20:28Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
28 Ine ndinawalowetsa mʼdziko limene ndinalumbira kuti ndidzawapatsa.+ Koma ataona mapiri onse ataliatali ndi mitengo ya masamba ambiri,+ anayamba kupereka nsembe zawo ndi zopereka zawo zimene sizinkandisangalatsa. Anapereka kafungo kosangalatsa* ka nsembe zawo ndiponso kuthira nsembe zawo zachakumwa pamalo amenewo.
-