-
Yeremiya 6:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Kodi iwo amachita manyazi ndi zinthu zonyansa zimene achita?
Iwo sachita manyazi ngakhale pangʼono,
Ndipo sadziwa nʼkomwe kuchita manyazi.+
Choncho iwo adzagwa pamodzi ndi anthu amene akugwa.
Ndikamadzawapatsa chilango, iwo adzapunthwa,” akutero Yehova.
-