-
Deuteronomo 30:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Yehova Mulungu wanu adzakubweretsani mʼdziko limene makolo anu analitenga kuti likhale lawo, ndipo lidzakhala lanu. Iye adzachititsa kuti zinthu zikuyendereni bwino ndipo adzakuchulukitsani kwambiri kuposa makolo anu.+
-
-
Zekariya 10:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 ‘Ndidzawaitana ndi likhweru nʼkuwasonkhanitsa pamodzi.
Popeza ndidzawawombola,+ iwo adzachuluka.
Ndipo adzapitiriza kuchuluka.
-