Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Ekisodo 14:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mafumu 19:17-19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Nʼzoonadi Yehova, kuti mafumu a Asuri awononga mayiko ndi anthu a mʼmayikowo.+ 18 Aponya milungu yawo pamoto, chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala. Nʼchifukwa chake anatha kuiwononga. 19 Tsopano inu Yehova Mulungu wathu, chonde tipulumutseni mʼmanja mwake, kuti maufumu onse apadziko lapansi adziwe kuti inu nokha Yehova, ndinu Mulungu.”+

  • Salimo 83:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Ezekieli 39:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 ‘Ndidzasonyeza ulemerero wanga pakati pa anthu a mitundu ina ndipo mitundu yonse ya anthu idzaona chiweruzo chimene ndapereka komanso mphamvu zimene* ndasonyeza pakati pawo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani