Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 2 Mbiri 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako, mfumu ya Iguputo inaika Eliyakimu, mʼbale wake wa Yehoahazi, kukhala mfumu ya Yuda ndi Yerusalemu ndipo inamusintha dzina kuti akhale Yehoyakimu. Koma Neko+ anatenga Yehoahazi, mʼbale wake wa Eliyakimu, nʼkupita naye ku Iguputo.+

  • Yeremiya 22:18, 19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho ponena za Yehoyakimu+ mwana wa Yosiya, mfumu ya Yuda, Yehova wanena kuti,

      ‘Sadzamulira ngati mmene anthu amachitira kuti:

      “Mayo ine mchimwene wanga! Mayo ine mchemwali wanga!”

      Sadzamulira kuti:

      “Mayo ine mbuye wanga! Mayo ine a mfumu aja!”

      19 Adzaikidwa mʼmanda ngati mmene amaikira bulu,+

      Adzamukoka kudutsa naye pamageti a Yerusalemu

      Nʼkukamutaya kunja.’+

  • Yeremiya 36:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Choncho ponena za chilango chimene adzapatse Yehoyakimu mfumu ya Yuda, Yehova wanena kuti, ‘Sipadzapezeka mwana wake aliyense wokhala pampando wachifumu wa Davide+ ndipo mtembo wake udzakhala padzuwa lotentha masana ndipo usiku udzakhala panja pozizira.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani