Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 47:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Alangizi ako ambirimbiri akutopetsa.

      Anthu amene amalambira zinthu zakumwamba,* amene amayangʼanitsitsa nyenyezi,+

      Amene amakudziwitsa zimene zikuchitikire

      Mwezi watsopano ukaoneka,

      Auze abwere adzakupulumutse.

  • Danieli 2:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Danieli anayankha mfumuyo kuti: “Palibe amuna anzeru, anthu olankhula ndi mizimu, ansembe ochita zamatsenga kapena anthu okhulupirira nyenyezi amene angakwanitse kukuuzani inu mfumu chinsinsi chimene mukufuna kudziwa.+

  • Danieli 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Amuna onse anzeru anabwera kwa mfumu koma sanathe kuwerenga mawu amene analembedwawo kapena kuuza mfumu kumasulira kwake.+

  • Danieli 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ineyo anandibweretsera amuna anzeru ndi anthu okhulupirira mizimu kuti awerenge mawu amene alembedwawa nʼkundiuza kumasulira kwake, koma iwo alephera kumasulira uthenga wake.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani