Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Deuteronomo 28:45
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • 2 Mafumu 17:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Ezekieli 23:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Wamkulu dzina lake anali Ohola,* wamngʼono anali Oholiba.* Akazi amenewa anakhala anga ndipo anabereka ana aamuna ndi aakazi. Ohola akuimira Samariya+ ndipo Oholiba akuimira Yerusalemu.

      5 Ohola anayamba kuchita uhule+ ngakhale kuti anali mkazi wanga. Ankalakalaka kugona ndi amuna amene ankamukonda kwambiri+ omwe ndi Asuri amene ankakhala moyandikana naye.+

  • Hoseya 4:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tamverani mawu a Yehova inu Aisiraeli.

      Yehova ali ndi mlandu ndi anthu amʼdzikoli,+

      Chifukwa mʼdzikoli mulibe choonadi, chikondi chokhulupirika ndipo anthu ake sadziwa Mulungu.+

       2 Kulumbira monama, bodza,+ kuphana,+

      Kuba ndi chigololo+ zafala mʼdzikoli.

      Ndipo kukhetsa magazi kukuchitika pafupipafupi.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani