Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 38:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiye ndinati, ‘Ukhoza kufika apa, koma usapitirirepo,

      Ndipo mafunde ako aatali azilekezera pamenepaʼ?+

  • Salimo 104:6, 7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Munaliphimba ndi madzi ozama ngati kuti mwaliphimba ndi nsalu.+

      Madziwo anakwera kupitirira mapiri.

       7 Chifukwa cha kudzudzula kwanu, madziwo anathawa.+

      Atamva mabingu anu anayamba kuthawa mopanikizika kwambiri

  • Salimo 107:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Iye amachititsa kuti mphepo yamkuntho ikhale bata,

      Mafunde apanyanja amadekha.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani