-
Levitiko 22:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Musamapereke nsembe nyama iliyonse yachilema,+ chifukwa Mulungu sangasangalale nanu.
-
-
Deuteronomo 15:21Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
21 Koma ngati nyamayo ili ndi vuto, monga kulumala kapena khungu, kapena chilema chilichonse chachikulu, musamaipereke nsembe kwa Yehova Mulungu wanu.+
-