Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yeremiya 49:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano amuna inu, tamverani zimene Yehova wasankha* kuchitira Edomu ndiponso zimene waganiza kuti achitire anthu amene akukhala ku Temani:+

      Ndithudi, chilombo chidzakokera kutali ana a nkhosa.

      Adzachititsa kuti malo awo okhala asanduke bwinja chifukwa cha zimene anthuwo anachita.+

  • Yoweli 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma Iguputo adzasanduka bwinja,+

      Ndipo Edomu adzakhala chipululu chopanda kanthu.+

      Chifukwa cha nkhanza zimene anachitira anthu a ku Yuda,+

      Ndiponso chifukwa chokhetsa magazi a anthu osalakwa mʼdziko la Yudalo.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani