Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yesaya 34:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Usiku kapena masana motowo sudzazimitsidwa.

      Utsi wake udzapitiriza kukwera mʼmwamba mpaka kalekale.

      Dzikolo lidzakhala lowonongedwa ku mibadwomibadwo.

      Mpaka muyaya, palibe amene adzadutsemo.+

  • Yesaya 34:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Minga zidzamera pansanja zake zokhala ndi mpanda wolimba,

      Zomera zoyabwa ndi zitsamba zaminga zidzamera pamalo ake otetezeka.

      Iye adzakhala malo okhala mimbulu,+

      Ndi malo obisalamo nthiwatiwa.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani