-
Yeremiya 27:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 ‘Ine sindinawatume,’ akutero Yehova, ‘koma iwo akulosera zabodza mʼdzina langa. Mukawamvera ndidzakubalalitsani ndipo ndidzawononga inuyo limodzi ndi aneneri amene akulosera kwa inu.’”+
-