Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • 1 Mafumu 22:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho Mikaya anati: “Ndikuona Aisiraeli onse atabalalika mʼmapiri+ ngati nkhosa zopanda mʼbusa. Ndipo Yehova anati: ‘Amenewa alibe mtsogoleri. Aliyense abwerere kunyumba kwake mwamtendere.’”

  • Yesaya 53:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Tonsefe tikungoyendayenda uku ndi uku ngati nkhosa zosochera.+

      Aliyense akulowera njira yake

      Ndipo Yehova wachititsa kuti zolakwa za tonsefe zigwere pa ameneyo.+

  • Ezekieli 34:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Choncho zinamwazikana chifukwa zinalibe mʼbusa+ ndipo zinakhala chakudya cha zilombo zonse zakutchire.

  • Ezekieli 34:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 ‘“Pali ine Mulungu wamoyo,” akutero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, “nkhosa zanga zagwidwa ndipo zakhala chakudya cha zilombo zonse zakutchire chifukwa panalibe mʼbusa ndipo abusa anga sanazifunefune. Koma ankangodzidyetsa okha, osadyetsa nkhosa zanga.”’

  • Mateyu 9:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani