-
1 Mafumu 17:9, 10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 “Nyamuka, upite ku Zarefati mʼdziko la Sidoni ukakhale kumeneko. Ine ndikalamula mayi wamasiye kuti azikakupatsa chakudya.”+ 10 Choncho Eliya ananyamuka nʼkupita ku Zarefati. Atafika pageti la mzindawo anaona mayi wamasiye akutola nkhuni. Ndiyeno anamuitana nʼkumuuza kuti: “Mundipatseko madzi pangʼono mʼkapu kuti ndimwe.”+
-