Yesaya 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Choncho Yehova akupatsani chizindikiro: Tamverani! Mtsikana* adzakhala woyembekezera ndipo adzabereka mwana wamwamuna.+ Mwanayo adzamʼpatsa dzina lakuti Emanueli.*+ Mateyu 1:24, 25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
14 Choncho Yehova akupatsani chizindikiro: Tamverani! Mtsikana* adzakhala woyembekezera ndipo adzabereka mwana wamwamuna.+ Mwanayo adzamʼpatsa dzina lakuti Emanueli.*+