Salimo 69:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Mayina awo afufutidwe mʼbuku la anthu amoyo,*+Ndipo iwo asalembedwe mʼbuku limene muli mayina a anthu olungama.+ Luka 10:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
28 Mayina awo afufutidwe mʼbuku la anthu amoyo,*+Ndipo iwo asalembedwe mʼbuku limene muli mayina a anthu olungama.+