Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Yobu 39:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kapena kodi chiwombankhanga chimauluka mʼmwamba chifukwa choti iweyo wachilamula,+

      Nʼkukamanga chisa chake pamwamba kwambiri?+

  • Yobu 39:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Chili pamalo omwewo, chimafunafuna chakudya,+

      Maso ake amaona kutali kwambiri.

  • Ezekieli 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Nkhope za angelowo zinkaoneka chonchi: Mngelo aliyense pa angelo 4 amenewo anali ndi nkhope ya munthu, nkhope ya mkango+ mbali yakumanja ndiponso nkhope ya ngʼombe+ yamphongo mbali yakumanzere. Mngelo aliyense pa angelo 4 amenewo analinso ndi nkhope+ ya chiwombankhanga.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani