Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Zimene Zili M‘buku la Yoweli

YOWELI

ZIMENE ZILI MʼBUKULI

  • 1

    • Mliri woopsa wa ziwala ndi dzombe (1-14)

    • “Tsiku la Yehova lili pafupi” (15-20)

      • Mneneri anaitana Yehova (19, 20)

  • 2

    • Tsiku la Yehova komanso gulu lalikulu la asilikali ake (1-11)

    • Anawauza kuti abwerere kwa Yehova (12-17)

      • “Ngʼambani mitima yanu” (13)

    • Yehova anayankha anthu ake (18-32)

      • “Ndidzapereka mzimu wanga”  (28)

      • Zodabwitsa kumwamba ndi padziko lapansi (30)

      • Oitana pa dzina la Yehova adzapulumuka (32)

  • 3

    • Yehova adzaweruza mitundu yonse ya anthu (1-17)

      • Chigwa cha Yehosafati (2, 12)

      • Chigwa choweruzira (14)

      • Yehova, malo othawirako a Isiraeli (16)

    • Yehova adzadalitsa anthu ake (18-21)

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani